Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 6:40 - Buku Lopatulika

40 Ndipo anakhala pansi mabungwemabungwe a makumi khumi, ndi a makumi asanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

40 Ndipo anakhala pansi mabungwemabungwe a makumi khumi, ndi a makumi asanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

40 Anthu aja adakhaladi pansi, m'magulu mwina anthu makumi khumi, mwina anthu makumi asanu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

40 Ndipo anakhala pansi mʼmagulu a anthu 100 ndi gulu la anthu makumi asanu.

Onani mutuwo Koperani




Marko 6:40
3 Mawu Ofanana  

Ndipo anawalamulira kuti akhalitse pansi onse magulumagulu pamsipu.


Ndipo Iye anatenga mikate isanuyo ndi nsomba ziwirizo nayang'ana kumwamba, nadalitsa, nagawa mikate; napatsa kwa ophunzira kuti apereke kwa iwo; ndi nsomba ziwiri anagawira onsewo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa