Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 6:39 - Buku Lopatulika

39 Ndipo anawalamulira kuti akhalitse pansi onse magulumagulu pamsipu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

39 Ndipo anawalamulira kuti akhalitse pansi onse magulumagulu pamsipu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

39 Tsono Yesu adalamula kuti anthu onse aja akhale pansi m'magulumagulu pa msipu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

39 Pamenepo Yesu anawalamulira kuti awakhazike anthu pansi mʼmagulu pa msipu obiriwira.

Onani mutuwo Koperani




Marko 6:39
9 Mawu Ofanana  

ndi zakudya za pa gome lake, ndi makhalidwe a anyamata ake, ndi maimiriridwe a atumiki ake, ndi zovala zao, ndi otenga zikho ake, ndi nsembe yake yopsereza imene amapereka m'nyumba ya Yehova, anakhululuka malungo.


Ndipo Iye analamulira anthuwo akhale pansi onse;


Ndipo Iye ananena nao, kuti, Muli nayo mikate ingati? Pitani, mukaone. Ndipo m'mene anadziwa ananena, Isanu, ndi nsomba ziwiri.


Ndipo anakhala pansi mabungwemabungwe a makumi khumi, ndi a makumi asanu.


Pakuti anali amuna ngati zikwi zisanu. Koma Iye anati kwa ophunzira ake, Khalitsani iwo pansi magulumagulu, ngati makumi asanuasanu.


Nati Yesu, Akhalitseni anthu pansi. Ndipo panali udzu wambiri pamalopo. Pamenepo amunawo anakhala pansi, kuwerenga kwao monga zikwi zisanu.


pakuti Mulungu sali Mulungu wa chisokonezo koma wa mtendere; monga mwa Mipingo yonse ya oyera mtima.


Koma zonse zichitike koyenera ndi kolongosoka.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa