Marko 6:36 - Buku Lopatulika36 muwauze kuti amuke, alowe kuminda ndi kumidzi yozungulira, akadzigulire okha kanthu kakudya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201436 muwauze kuti amuke, alowe kumilaga ndi kumidzi yozungulira, akadzigulire okha kanthu kakudya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa36 Auzeni anthuŵa azipita, anke ku midzi ili pafupiyi kuti azikagula chakudya.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero36 Awuzeni anthuwa azipita ku midzi ndi madera ozungulira, kuti akadzigulire kanthu kakuti adye.” Onani mutuwo |