Marko 6:32 - Buku Lopatulika32 Ndipo anachokera m'ngalawa kunka kumalo achipululu padera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 Ndipo anachokera m'ngalawa kunka kumalo achipululu padera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Tsono adaloŵa m'chombo napita kwaokha kumalo kosapitapita anthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 Ndipo anachoka okha pa bwato napita kumalo a okhaokha. Onani mutuwo |