Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 6:29 - Buku Lopatulika

29 Ndipo m'mene ophunzira ake anamva, anadza nanyamula mtembo wake nauika m'manda.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

29 Ndipo m'mene ophunzira ake anamva, anadza nanyamula mtembo wake nauika m'manda.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

29 Ophunzira a Yohane atamva zimenezi, adabwera nadzatenga mtembo wake nkukauika m'manda.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

29 Atamva izi, ophunzira a Yohane anabwera nadzatenga mtembo ndi kukawuyika mʼmanda.

Onani mutuwo Koperani




Marko 6:29
7 Mawu Ofanana  

Ndipo anamuika m'mzinda wa Davide, pakati pa mafumu; pakuti anachita zabwino mu Israele, ndi kwa Mulungu, ndi kunyumba yake.


Ndipo ophunzira ake anadza, natola mtembo, nauika; ndipo anadza nauza Yesu.


natengera mutu wake mumbale, naupereka kwa buthulo; ndipo buthu linaupereka kwa amake.


Ndipo atumwi anasonkhana kwa Yesu; namuuza zilizonse adazichita, ndi zonse adaziphunzitsa.


Ndipo anamuika Stefano anthu opembedza, namlira maliro aakulu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa