Marko 6:24 - Buku Lopatulika24 Ndipo anatuluka, nati kwa amake, Ndidzapempha chiyani? Ndipo iye anati, Mutu wake wa Yohane Mbatizi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Ndipo anatuluka, nati kwa amake, Ndidzapempha chiyani? Ndipo iye anati, Mutu wake wa Yohane Mbatizi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Mtsikanayo adatuluka nakafunsa mai wake kuti, “Kodi ndikapemphe chiyani?” Mai wakeyo adati “Kapemphe mutu wa Yohane Mbatizi.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Iye anatuluka nati kwa amayi ake, “Kodi ndikapemphe chiyani?” Iye anamuyankha kuti, “Mutu wa Yohane Mʼbatizi.” Onani mutuwo |