Marko 6:19 - Buku Lopatulika19 Ndipo Herodiasi anamuda, nafuna kumupha; koma sanakhoze; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Ndipo Herodiasi anamuda, nafuna kumupha; koma sanakhoze; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Tsono Herodiasiyo ankadana naye Yohane, ndipo ankafuna kuti aphedwe basi. Koma ankalephera, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Ndipo Herodia anamusungira Yohane chidani ndipo anafuna kumupha, koma sanathe kutero, Onani mutuwo |