Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 6:18 - Buku Lopatulika

18 Pakuti Yohane adanena kwa Herode, Si kuloledwa kwa inu kukhala naye mkazi wa mbale wanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Pakuti Yohane adanena kwa Herode, Si kuloledwa kwa inu kukhala naye mkazi wa mbale wanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Ndipo Yohane adaamuuza kuti, “Nkulakwira Malamulo kulanda mkazi wa mbale wanu.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Pakuti Yohane ankanena kwa Herode kuti, “Sikololedwa kwa inu kuti mukwatire mkazi wa mʼbale wanu.”

Onani mutuwo Koperani




Marko 6:18
8 Mawu Ofanana  

Koma Mikaya anati, Pali Yehova, zimene Yehova adzanena nane ndidzanena ine.


Usamavula mkazi wa mbale wako; ndiye thupi la mbale wako.


Munthu akatenga mkazi wa mbale wake, chodetsa ichi; wavula mbale wake; adzakhala osaona ana.


Namthira malovu, natenga bango, nampanda Iye pamutu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa