Marko 6:15 - Buku Lopatulika15 Koma ena ananena, kuti, Ndiye Eliya. Anati enanso, Ndiye mneneri, monga ngati mmodzi wa aneneriwo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Koma ena ananena, kuti, Ndiye Eliya. Anati enanso, Ndiye mneneri, monga ngati mmodzi wa aneneriwo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Koma ena ankati, “Iyai, ameneyu ndi Eliya.” Enanso ankati, “Iyai, koma ndi mneneri wonga aneneri akale aja.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Ena anati, “Iye ndi Eliya.” Enanso anati, “Ndi mneneri, ofanana ndi mmodzi wa aneneri akale.” Onani mutuwo |