Marko 5:39 - Buku Lopatulika39 Ndipo m'mene atalowa, ananena nao, Mubuma ndi kulira bwanji? Mwana sanafe, koma ali m'tulo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201439 Ndipo m'mene atalowa, ananena nao, Mubuma ndi kulira bwanji? Mwana sanafe, koma ali m'tulo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa39 Iye ataloŵa, adaŵafunsa kuti, “Chifukwa chiyani mukuchita phokoso lonseli ndi kubuma? Mwanayutu sadamwalire ai, ali m'tulo chabe.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero39 Analowa nati kwa iwo, “Mukuchita phokoso ndi kulira chifukwa chiyani? Mwanayu sanamwalire koma ali mtulo.” Onani mutuwo |