Marko 5:38 - Buku Lopatulika38 Ndipo anafika kunyumba kwake kwa mkulu wa sunagoge; ndipo anaona chipiringu, ndi ochita maliro, ndi akukuwa ambiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201438 Ndipo anafika kunyumba kwake kwa mkulu wa sunagoge; ndipo anaona chipiringu, ndi ochita maliro, ndi akukuwa ambiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa38 Pamene iwo adafika kunyumba kwa mkulu wa nyumba yamapemphero uja, Yesu adaona chipiringu cha anthu, akulira ndi kubuma. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero38 Atafika ku nyumba ya mkulu wa sunagoge, Yesu anaona chipiringu cha anthu akulira ndi kufuwula kwambiri. Onani mutuwo |