Marko 5:37 - Buku Lopatulika37 Ndipo sanalole munthu yense kutsagana naye, koma Petro, ndi Yakobo, ndi Yohane mbale wake wa Yakobo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201437 Ndipo sanalole munthu yense kutsagana naye, koma Petro, ndi Yakobo, ndi Yohane mbale wake wa Yakobo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa37 Tsono sadalole kuti winanso atsagane naye, koma Petro, ndi Yakobe, ndi Yohane, mbale wa Yakobeyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero37 Iye sanalole munthu wina aliyense kuti amutsatire koma Petro, Yakobo ndi Yohane mʼbale wa Yakobo. Onani mutuwo |