Marko 5:36 - Buku Lopatulika36 Koma Yesu wosasamala mau olankhulidwawo, ananena kwa mkulu wa sunagoge, Usaope, khulupirira kokha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201436 Koma Yesu wosasamala mau olankhulidwawo, ananena kwa mkulu wa sunagoge, Usaope, khulupirira kokha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa36 Koma Yesu sadasamale zimene anthuwo ankanena. Adauza mkulu uja kuti, “Musaope ai, inu mungokhulupirira.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero36 Posasamala zomwe ananena, Yesu anamuwuza mkulu wa sunagoge uja kuti, “Usachite mantha; ingokhulupirira.” Onani mutuwo |