Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 5:28 - Buku Lopatulika

28 Pakuti ananena iye, Ngati ndikakhudza ngakhale zovala zake ndidzapulumutsidwa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

28 Pakuti ananena iye, Ngati ndikakhudza ngakhale zovala zake ndidzapulumutsidwa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

28 Mumtima mwake ankaganiza kuti, “Ndikangokhudza ngakhale zovala zake zokhazo, ndichira.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

28 chifukwa anaganiza kuti, “Ngati nditangokhudza mkanjo wake, ndidzachiritsidwa.”

Onani mutuwo Koperani




Marko 5:28
2 Mawu Ofanana  

m'mene iye anamva mbiri yake ya Yesu, anadza m'khamu kumbuyo kwake, nakhudza chovala chake.


Ndipo pomwepo kasupe wa nthenda yake adaphwa; ndipo anazindikira m'thupi kuti anachiritsidwa chivutiko chake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa