Marko 5:27 - Buku Lopatulika27 m'mene iye anamva mbiri yake ya Yesu, anadza m'khamu kumbuyo kwake, nakhudza chovala chake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 m'mene iye anamva mbiri yake ya Yesu, anadza m'khamu kumbuyo kwake, nakhudza chovala chake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Maiyo anali atamva za Yesu. Tsono adaloŵa m'chinamtindi cha anthu chija, nkuphaphatiza mpaka kukafika cha kumbuyo kwa Yesu, nakhudza chovala chake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Atamva za Yesu, anabwera kumbuyo kwake mʼgulu la anthu ndipo anakhudza mkanjo wake, Onani mutuwo |