Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 5:17 - Buku Lopatulika

17 Ndipo anayamba kumpempha Iye kuti achoke m'malire ao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Ndipo anayamba kumpempha Iye kuti achoke m'malire ao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Apo anthuwo adampempha Yesu kuti achoke ku dera laolo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Ndipo anthu anayamba kumupempha Yesu kuti achoke mʼdera lawo.

Onani mutuwo Koperani




Marko 5:17
10 Mawu Ofanana  

Ndipo Abimeleki anati kwa Isaki, Uchoke kwa ife chifukwa kuti iwe uli wamphamvu wopambana ife.


Ndipo mkaziyo ananena ndi Eliya, Ndili nawe chiyani munthu iwe wa Mulungu? Kodi wadza kwa ine kundikumbutsa tchimo langa, ndi kundiphera mwana wanga?


Ndipo onani, mzinda wonse unatulukira kukakumana naye Yesu, ndipo m'mene anamuona Iye, anampempha kuti achoke m'malire ao.


Kuti, Tili ndi chiyani ife ndi Inu Yesu wa ku Nazarete? Kodi mwadza kudzationonga ife: Ndikudziwani, ndinu Woyerayo wa Mulungu.


ndipo anafuula ndi mau olimba, nanena, Ndili ndi chiyani ine ndi Inu, Yesu Mwana wa Mulungu Wamkulukulu? Ndikulumbirirani pa Mulungu, msandizunze.


Koma Simoni Petro, pamene anaona, anagwa pansi pa mawondo ake a Yesu, nanena, Muchoke kwa ine, Ambuye, chifukwa ndine munthu wochimwa.


Ndipo anthu aunyinji onse a dziko la Agerasa loyandikira anamfunsa Iye achoke kwa iwo; chifukwa anagwidwa ndi mantha aakulu. Ndipo Iye analowa m'ngalawa, nabwerera.


Ndipo anadza nawapembedza; ndipo pamene anawatulutsa, anawapempha kuti achoke pamzinda.


Ndipo tsopano tiferenji? Popeza moto waukulu uwu udzatitha. Tikaonjeza kumva mau a Yehova Mulungu wathu, tidzafa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa