Marko 4:31 - Buku Lopatulika31 Ngati mbeu yampiru, imene ikafesedwa panthaka, ingakhale ichepa ndi mbeu zonse za padziko, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Ngati mbeu yampiru, imene ikafesedwa panthaka, ingakhale ichepa ndi mbeu zonse za padziko, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Uli ngati njere ya mbeu ya mpiru. Pamene aifesa m'nthaka, ndi yaing'ono kwambiri mukaiyerekeza ndi njere zina pansi pano. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Uli ngati mbewu ya mpiru imene ndi mbewu yayingʼono kwambiri yomwe mumadzala mʼnthaka. Onani mutuwo |