Marko 3:35 - Buku Lopatulika35 Pakuti aliyense achita chifuniro cha Mulungu, yemweyo ndiye mbale wanga, ndi mlongo, ndi amai. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201435 Pakuti aliyense achita chifuniro cha Mulungu, yemweyo ndiye mbale wanga, ndi mlongo, ndi amai. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa35 Aliyense wochita zimene Mulungu akufuna, ameneyo ndiye mbale wanga ndi mlongo wanga ndi amai anga.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero35 Aliyense amene achita chifuniro cha Mulungu ndi mʼbale wanga ndi mlongo wanga ndi amayi anga.” Onani mutuwo |