Marko 3:28 - Buku Lopatulika28 Indetu, ndinena ndi inu, Adzakhululukidwa machimo onse a ana a anthu, ndi zamwano zilizonse adzachita mwano nazo; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Indetu, ndinena ndi inu, Adzakhululukidwa machimo onse a ana a anthu, ndi zamwano zilizonse adzachita mwano nazo; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 “Ndithu ndikunenetsa kuti anthu angathe kukhululukidwa machimo onse, ngakhalenso zonena zao zonse zomunyoza Mulunguyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Ndikukuwuzani zoona kuti machimo onse ndi zamwano zonse za anthu zidzakhululukidwa, Onani mutuwo |