Marko 2:20 - Buku Lopatulika20 Koma adzadza masiku, pamene mkwati adzachotsedwa kwa iwo, ndipo pamenepo adzasala kudya tsiku lomwelo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Koma adzadza masiku, pamene mkwati adzachotsedwa kwa iwo, ndipo pamenepo adzasala kudya tsiku lomwelo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Koma idzafika nthaŵi pamene adzaŵachotsere mkwatiyo. Pamenepo ndiye azidzasala zakudya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Koma nthawi idzafika pamene mkwati adzachotsedwa pakati pawo, ndipo pa tsiku limenelo adzasala kudya. Onani mutuwo |