Marko 16:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo iwowa anachoka nawauza otsala; koma iwo omwe sanawavomereze. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo iwowa anachoka nawauza otsala; koma iwo omwe sanawavomereze. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Ophunzirawo adabwerera kudzauza anzao aja, koma iwonso sadaŵakhulupirire. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Iwo anabwerera ndi kudzawawuza enawo; koma iwo sanakhulupirirebe. Onani mutuwo |