Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 16:13 - Buku Lopatulika

13 Ndipo iwowa anachoka nawauza otsala; koma iwo omwe sanawavomereze.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Ndipo iwowa anachoka nawauza otsala; koma iwo omwe sanawavomereze.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Ophunzirawo adabwerera kudzauza anzao aja, koma iwonso sadaŵakhulupirire.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Iwo anabwerera ndi kudzawawuza enawo; koma iwo sanakhulupirirebe.

Onani mutuwo Koperani




Marko 16:13
9 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene anamuona Iye, anamlambira; koma ena anakayika.


Ndipo iwowo, pamene anamva kuti ali moyo, ndi kuti adapenyeka kwa iye, sanamvere.


Ndipo chitatha icho anaonekera kwa khumi ndi mmodzi iwo okha, alikuseama pachakudya; ndipo anawadzudzula chifukwa cha kusavomereza kwao ndi kuuma mtima, popeza sanavomereze iwo amene adamuona, atauka Iye.


Koma anati kwa iye, Ngati samvera Mose ndi aneneri, sadzakopeka mtima ngakhale wina akauka kwa akufa.


Ndipo mau awa anaoneka pamaso pao ngati nkhani zachabe, ndipo sanamvere akaziwo.


Koma pokhala iwo chikhalire osakhulupirira chifukwa cha chimwemwe, nalikuzizwa, anati kwa iwo, Muli nako kanthu kakudya kuno?


Chifukwa chake ophunzira ena ananena naye, Tamuona Ambuye. Koma iye anati kwa iwo, Ndikapanda kuona m'manja ake chizindikiro cha misomaliyo, ndi kuika chala changa m'chizindikiro cha misomaliyo, ndi kuika dzanja langa kunthiti yake; sindidzakhulupirira.


Pamenepo tsono analowanso wophunzira winayo, amene anayamba kufika kumanda, ndipo anaona, nakhulupirira.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa