Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 15:47 - Buku Lopatulika

47 Ndipo Maria wa Magadala ndi Maria amake wa Yosefe anapenya pomwe anaikidwapo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

47 Ndipo Maria wa Magadala ndi Maria amake wa Yosefe anapenya pomwe anaikidwapo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

47 Maria uja wa ku Magadala, ndi Maria mai wa Yosefe, ankaona kumene adamuika Yesu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

47 Mariya Magadalena ndi Mariya amayi a Yose anaona kumene anamuyika Yesu.

Onani mutuwo Koperani




Marko 15:47
8 Mawu Ofanana  

mwa iwo amene munali Maria wa Magadala, ndi Maria amake wa Yakobo, ndi wa Yosefe, ndi amake wa ana a Zebedeo.


Ndipo Maria wa Magadala anali pamenepo, ndi Maria winayo, anakhala pansi popenyana ndi mandawo.


Ndipo popita tsiku la Sabata, mbandakucha, tsiku lakuyamba la sabata, anadza Maria wa Magadala, ndi Maria winayo, kudzaona manda.


Ndipo analinso kumeneko akazi akuyang'anira kutali; mwa iwo anali Maria wa Magadala, ndi Maria amake wa Yakobo wamng'ono ndi wa Yosefe, ndi Salome;


Ndipo anagula bafuta, namtsitsa Iye, namkulunga m'bafutamo, namuika m'manda osemedwa m'thanthwe; nakunkhunizira mwala pakhomo la manda.


Ndipo litapita Sabata, Maria wa Magadala, ndi Maria amake wa Yakobo, ndi Salome, anagula zonunkhira, kuti akadze kumdzoza Iye.


Ndipo akazi, amene anachokera naye ku Galileya, anatsata m'mbuyo, naona manda, ndi maikidwe a mtembo wake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa