Marko 15:47 - Buku Lopatulika47 Ndipo Maria wa Magadala ndi Maria amake wa Yosefe anapenya pomwe anaikidwapo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201447 Ndipo Maria wa Magadala ndi Maria amake wa Yosefe anapenya pomwe anaikidwapo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa47 Maria uja wa ku Magadala, ndi Maria mai wa Yosefe, ankaona kumene adamuika Yesu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero47 Mariya Magadalena ndi Mariya amayi a Yose anaona kumene anamuyika Yesu. Onani mutuwo |