Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 15:36 - Buku Lopatulika

36 Ndipo anathamanga wina, nadzaza chinkhupule ndi vinyo wosasa, nachiika pabango, namwetsa Iye, nanena, Lekani; tione ngati Eliya adza kudzamtsitsa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

36 Ndipo anathamanga wina, nadzaza chinkhupule ndi vinyo wosasa, nachiika pabango, namwetsa Iye, nanena, Lekani; tione ngati Eliya adza kudzamtsitsa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

36 Motero wina adathamanga nakaviika chinkhupule m'vinyo wosasa, nkuchitsomeka ku bango nampatsira, kuti amwe. Anzakewo adati, “Taima, tiwone ngati Eliyayo abweredi kudzamtsitsa.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

36 Munthu wina anathamanga, natenga chinkhupule atachiviyika mu vinyo wosasa, anachizika ku mtengo, ndi kumupatsa Yesu kuti amwe. Munthuyo anati, “Musiyeni yekha tsopano. Tiyeni tione ngati Eliya angabwere kudzamutsitsa.”

Onani mutuwo Koperani




Marko 15:36
7 Mawu Ofanana  

Ndipo anandipatsa ndulu ikhale chakudya changa; nandimwetsa vinyo wosasa pomva ludzu ine.


Ndipo pomwepa mmodzi wa iwo anathamanga, natenga chinkhupule, nachidzaza ndi vinyo wosasa, nachiika pabango, namwetsa Iye.


Ndipo anampatsa vinyo wosakaniza ndi mure; koma Iye sanamlandire.


Ndipo ena akuimirirapo, pakumva, ananena, Taonani, aitana Eliya.


Ndipo Yesu anatulutsa mau okweza, napereka mzimu wake.


Ndipo asilikalinso anamnyoza, nadza kwa Iye, nampatsa vinyo wosasa,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa