Marko 15:34 - Buku Lopatulika34 Ndipo pa ora lachisanu ndi chinai Yesu anafuula ndi mau okweza, Eloi, Eloi, lama sabakitani? ndiko kusandulika, Mulungu wanga, Mulungu wanga mwandisiyiranji Ine? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 Ndipo pa ora lachisanu ndi chinai Yesu anafuula ndi mau okweza, Eloi, Eloi, lama sabakitani? ndiko kusandulika, Mulungu wanga, Mulungu wanga mwandisiyiranji Ine? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Tsono nthaŵi ili 3 koloko, Yesu adafuula kwakukulu kuti, “Eloi, Eloi, lama sabakatani?” Ndiye kuti, “Mulungu wanga, Mulungu wanga, mwandisiyiranji?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Pa ora lachisanu ndi chinayi Yesu analira mofuwula kuti, “Eloi, Eloi, lama sabakitani?” Kutanthauza kuti, “Mulungu wanga, Mulungu wanga, mwandisiyiranji Ine?” Onani mutuwo |