Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 15:31 - Buku Lopatulika

31 Moteronso ansembe aakulu anamtonza mwa iwo okha pamodzi ndi alembi, nanena, Anapulumutsa ena; sangathe kudzipulumutsa yekha.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

31 Moteronso ansembe aakulu anamtonza mwa iwo okha pamodzi ndi alembi, nanena, Anapulumutsa ena; sakhoza kudzipulumutsa yekha.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

31 Nawonso akulu a ansembe ankamuseka, nkumauzana ndi aphunzitsi a Malamulo kuti, “Adapulumutsa anthu ena, koma akulephera kudzipulumutsa Iye yemwe!

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

31 Chimodzimodzinso akulu a ansembe ndi aphunzitsi amalamulo anamunyoza Iye pakati pawo. Iwo anati, “Anapulumutsa ena, koma sangathe kudzipulumutsa yekha!

Onani mutuwo Koperani




Marko 15:31
8 Mawu Ofanana  

udzipulumutse mwini, nutsike pamtanda.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa