Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 15:30 - Buku Lopatulika

30 udzipulumutse mwini, nutsike pamtanda.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 udzipulumutse mwini, nutsike pamtanda.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 Tadzipulumutsatu, tsika pamtandapo!”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 tsika kuchoka pa mtandapo ndipo udzipulumutse wekha!”

Onani mutuwo Koperani




Marko 15:30
3 Mawu Ofanana  

Adadzitengera kwa Yehova; kuti adzampulumutsa, amlanditse tsopano popeza akondwera naye.


Ndipo iwo akupitirirapo anamchitira mwano, napukusa mitu yao, nanena, Ha! Iwe wakupasula Kachisi, ndi kummanga masiku atatu,


Moteronso ansembe aakulu anamtonza mwa iwo okha pamodzi ndi alembi, nanena, Anapulumutsa ena; sangathe kudzipulumutsa yekha.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa