Marko 15:27 - Buku Lopatulika27 Ndipo anapachika pamodzi ndi Iye achifwamba awiri; mmodzi kudzanja lake lamanja ndi wina kulamanzere. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Ndipo anapachika pamodzi ndi Iye achifwamba awiri; mmodzi kudzanja lake lamanja ndi wina kulamanzere. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Pamodzi ndi Yesu adaapachikanso pa mitanda zigaŵenga ziŵiri, china ku dzanja lamanja, china ku dzanja lamanzere. [ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Achifwamba awiri anapachikidwanso pamodzi ndi Iye, wina kumanja kwake ndi wina kumanzere kwake. Onani mutuwo |