Marko 15:24 - Buku Lopatulika24 Ndipo anampachika Iye, nagawana zovala zake mwa iwo okha, ndi kuchita maere pa izo, kuti adziwe yense adzatenga chiyani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Ndipo anampachika Iye, nagawana zovala zake mwa iwo okha, ndi kuchita maere pa izo, kuti adziwe yense adzatenga chiyani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Atampachika pa mtanda, adagaŵana zovala zake. Adaachita maere kuti aone zimene aliyense atenge. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Ndipo anamupachika Iye. Anachita maere ogawana zovala zake kuti aone chimene aliyense angatenge. Onani mutuwo |