Marko 15:23 - Buku Lopatulika23 Ndipo anampatsa vinyo wosakaniza ndi mure; koma Iye sanamlandire. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Ndipo anampatsa vinyo wosanganiza ndi mure; koma Iye sanamlandire. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Adaafuna kumpatsa vinyo wosanganiza ndi mure kuti amwe, koma Iye adakana. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Kenaka anamupatsa Iye vinyo wosakaniza ndi mure, koma Iye sanamwe. Onani mutuwo |