Marko 15:20 - Buku Lopatulika20 Ndipo atatha kumnyoza anamvula chibakuwacho namveka Iye zovala zake. Ndipo anatuluka naye kuti akampachike Iye pamtanda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Ndipo atatha kumnyoza anamvula chibakuwacho namveka Iye zovala zake. Ndipo anatuluka naye kuti akampachike Iye pamtanda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Ataseŵera naye mwachipongwe choncho, adamuvula chovala chija, namuvekanso zovala zake. Kenaka adamtenga, nkupita naye kuti akampachike pa mtanda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Ndipo anamuchita chipongwe, anamuvula mwinjiro wofiira uja ndi kumuveka zovala zake. Kenaka anamutenga kuti akamupachike. Onani mutuwo |