Marko 15:19 - Buku Lopatulika19 Ndipo anampanda Iye pamutu pake ndi bango, namthira malovu, nampindira maondo, namlambira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Ndipo anampanda Iye pamutu pake ndi bango, namthira malovu, nampindira maondo, namlambira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Ankamumenya m'mutu ndi ndodo, namamthira malovu, nkumamugwadira monyodola. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Ndipo anamugogoda pa mutu mobwerezabwereza ndi ndodo ndi kumulavulira. Anamugwadira ndi kumulambira Iye. Onani mutuwo |