Marko 15:18 - Buku Lopatulika18 Ndipo anayamba kumlankhula Iye, kuti, Tikuoneni, mfumu ya Ayuda! Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ndipo anayamba kumlankhula Iye, kuti, Tikuoneni, mfumu ya Ayuda! Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Kenaka adayamba kumampatsa moni kuti, “Tikuwoneni, mfumu ya Ayuda.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Ndipo anayamba kunena kwa lye kuti, “Ulemu kwa inu Mfumu ya Ayuda!” Onani mutuwo |