Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 15:18 - Buku Lopatulika

18 Ndipo anayamba kumlankhula Iye, kuti, Tikuoneni, mfumu ya Ayuda!

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Ndipo anayamba kumlankhula Iye, kuti, Tikuoneni, mfumu ya Ayuda!

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Kenaka adayamba kumampatsa moni kuti, “Tikuwoneni, mfumu ya Ayuda.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Ndipo anayamba kunena kwa lye kuti, “Ulemu kwa inu Mfumu ya Ayuda!”

Onani mutuwo Koperani




Marko 15:18
11 Mawu Ofanana  

Ndipo iye anafotokozera atate wake ndi abale ake; ndipo atate wake anamdzudzula, nati kwa iye, Loto limene walota iwe nlotani? Kodi ine ndi amai ako ndi abale ako tidzafika ndithu tokha kuweramira iwe pansi?


Tiyeni tsopano timuphe iye timponye m'dzenje, ndipo tidzati, Wajiwa ndi chilombo; ndipo tidzaona momwe adzachita maloto ake.


Ndipo analuka korona waminga, namveka pamutu pake, namgwiritsa bango m'dzanja lamanja lake; ndipo anagwada pansi pamaso pake, namchitira chipongwe, nati, Tikuoneni, mfumu ya Ayuda!


Ndipo anamveka Iye chibakuwa, naluka korona waminga, namveka pa Iye;


Ndipo anampanda Iye pamutu pake ndi bango, namthira malovu, nampindira maondo, namlambira.


Ndipo Pilato anamfunsa Iye, Kodi ndiwe mfumu ya Ayuda? Ndipo anayankha, nanena naye, Mwatero.


nadza kwa Iye, nanena, Tikuoneni, mfumu ya Ayuda! Nampanda khofu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa