Marko 15:14 - Buku Lopatulika14 Ndipo Pilato ananena nao, Pakuti Iye anachita choipa chotani? Koma iwo anafuulitsatu, Mpachikeni Iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ndipo Pilato ananena nao, Pakuti Iye anachita choipa chotani? Koma iwo anafuulitsatu, Mpachikeni Iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Pilato adaŵafunsa kuti, “Adalakwanji?” Koma iwo adafuula koposa kuti, “Mpachikeni pa mtanda!” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Pilato anafunsa kuti, “Chifukwa chiyani? Wapalamula mlandu wotani?” Koma anafuwula kwambiri, “Mpachikeni!” Onani mutuwo |