Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 15:13 - Buku Lopatulika

13 Ndipo anafuulanso, Mpachikeni pamtanda.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Ndipo anafuulanso, Mpachikeni pamtanda.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Anthuwo adafuula kuti, “Mpachikeni pa mtanda!”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Anafuwula kuti, “Mpachikeni!”

Onani mutuwo Koperani




Marko 15:13
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Pilato anawayankhanso, nati kwa iwo, Pamenepo ndidzachita chiyani ndi Iye amene mumtchula mfumu ya Ayuda?


Ndipo Pilato ananena nao, Pakuti Iye anachita choipa chotani? Koma iwo anafuulitsatu, Mpachikeni Iye.


koma iwo anafuula, nanena, Mpachikeni, mpachikeni pamtanda.


Ndipo ngakhale sanapeze chifukwa cha kumphera, anapempha Pilato kuti aphedwe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa