Marko 14:68 - Buku Lopatulika68 Koma anakana, nanena, Sindidziwa kapena kumvetsa chimene uchinena iwe; ndipo anatuluka kunka kuchipata; ndipo tambala analira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201468 Koma anakana, nanena, Sindidziwa kapena kumvetsa chimene uchinena iwe; ndipo anatuluka kunka kuchipata; ndipo tambala analira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa68 Koma Petro adakana, adati, “Zimenezo ine sindikuzidziŵa, sindikuzimvetsa konse.” Ndipo adatuluka kumapita cha ku chipata. Pamenepo tambala adalira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero68 Koma iye anakana nati, “Sindikudziwa kapena kumvetsetsa zimene ukuyankhula.” Ndipo anachoka napita ku chipata. Onani mutuwo |