Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 14:60 - Buku Lopatulika

60 Ndipo mkulu wa ansembe ananyamuka pakati, namfunsa Yesu, nanena, Suyankha kanthu kodi? Nchiyani ichi chimene awa alikuchitira mboni?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

60 Ndipo mkulu wa ansembe ananyamuka pakati, namfunsa Yesu, nanena, Suyankha kanthu kodi? Nchiyani ichi chimene awa alikuchitira mboni?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

60 Tsono mkulu wa ansembe onse adaimirira pamaso pao, nafunsa Yesu kuti, “Kodi ulibe poyankha? Nzotani zimene anthuŵa akukunenezazi?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

60 Kenaka mkulu wa ansembe anayimirira pakati pawo namufunsa Yesu kuti, “Kodi suyankha? Kodi umboni uwu ndi wotani umene anthu akukuchitira?”

Onani mutuwo Koperani




Marko 14:60
5 Mawu Ofanana  

Ndipo ngakhale momwemo umboni wao sunalingane.


Koma anakhala chete, osayankha kanthu. Mkulu wa ansembe anamfunsanso, nanena naye, Kodi Iwe ndiwe Khristu, Mwana wake wa Wolemekezeka?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa