Marko 14:52 - Buku Lopatulika52 koma iye anasiya nsaluyo, nathawa wamaliseche. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201452 koma iye anasiya bafutayo, nathawa wamaliseche. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa52 koma iye adaikolopola nsalu ija, nkuthaŵa ali maliseche. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero52 anathawa wamaliseche kusiya nsalu yake mʼmbuyo. Onani mutuwo |