Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 14:51 - Buku Lopatulika

51 Ndipo mnyamata wina anamtsata Iye, atafundira pathupi nsalu yabafuta yokha; ndipo anamgwira;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

51 Ndipo mnyamata wina anamtsata Iye, atafundira pathupi bafuta yekha; ndipo anamgwira;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

51 Mnyamata wina ankatsatira Yesu, atangofundira nsalu yokha, opanda chovala china. Anthu aja adaati amgwire,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

51 Mnyamata wamngʼono amene anangofundira nsalu yokha, wopanda chovala ankamutsatira Yesu. Atamugwira,

Onani mutuwo Koperani




Marko 14:51
4 Mawu Ofanana  

Ndipo mkazi anagwira iye chofunda chake, nati, Gona ndi ine; ndipo anasiya chofunda chake m'dzanja lake nathawa, natulukira kubwalo.


Ndipo iwo onse anamsiya Iye, nathawa.


koma iye anasiya nsaluyo, nathawa wamaliseche.


Nanena nao Samisoni, Mundilole ndikuphereni mwambi; mukanditanthauziratu uwu m'masiku asanuwa a madyerero, ndi kumasulira uwu, ndidzakupatsani malaya a nsalu yabafuta makumi atatu ndi zovala zosinthanitsa makumi atatu;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa