Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 14:47 - Buku Lopatulika

47 Koma mmodzi wina wa iwo akuimirirapo, anasolola lupanga lake, nakantha kapolo wake wa mkulu wa ansembe, namdula khutu lake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

47 Koma mmodzi wina wa iwo akuimirirapo, anasolola lupanga lake, nakantha kapolo wake wa mkulu wa ansembe, namdula khutu lake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

47 Koma wina mwa ophunzira amene anali naye pamenepo, adasolola lupanga lake, natema wantchito wa mkulu wa ansembe onse, mpaka kumusenga khutu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

47 Kenaka mmodzi wa iwo amene anayima pafupipo anatulutsa lupanga lake nakhapa wantchito wa wamkulu wa ansembe, nʼkudula khutu lake.

Onani mutuwo Koperani




Marko 14:47
5 Mawu Ofanana  

Ndipo anamthira manja, namgwira.


Ndipo Yesu anayankha nati kwa iwo, Kodi mwatuluka ndi malupanga ndi mikunkhu kundigwira Ine monga wachifwamba?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa