Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 14:42 - Buku Lopatulika

42 Ukani, tizimuka; onani wakundiperekayo ali pafupi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

42 Ukani, tizimuka; onani wakundiperekayo ali pafupi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

42 Dzukani, tiyeni tizipita. Suuyu wodzandipereka uja, wafika.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

42 Nyamukani! Tiyeni tizipita! Uyu wondipereka Ine wafika!”

Onani mutuwo Koperani




Marko 14:42
4 Mawu Ofanana  

Ukani, timuke; taonani, iye wakundipereka wayandikira.


Ndipo anadza kachitatu, nanena nao, Gonani tsopano, nimupumule; chakwanira; yafika nthawi; onani Mwana wa Munthu aperekedwa m'manja a anthu ochimwa.


Ndipo pomwepo, Iye ali chilankhulire, anadza Yudasi, mmodzi wa khumi ndi awiriwo, ndipo pamodzi naye khamu la anthu, ali nao malupanga ndi mikunkhu, ochokera kwa ansembe aakulu ndi alembi ndi akulu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa