Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 14:39 - Buku Lopatulika

39 Ndipo anachokanso, napemphera, nanena mau omwewo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

39 Ndipo anachokanso, napemphera, nanena mau omwewo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

39 Adachokanso nakapemphera ndi mau omwe aja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

39 Kenakanso anachoka ndi kukapemphera chimodzimodzi.

Onani mutuwo Koperani




Marko 14:39
7 Mawu Ofanana  

Ndipo popemphera musabwerezebwereze chabe iai, monga amachita anthu akunja, chifukwa ayesa kuti adzamvedwa ndi kulankhulalankhula kwao.


Dikirani, pempherani, kuti mungalowe m'kuyesedwa; mzimutu uli wakufuna, koma thupi lili lolefuka.


Ndipo anadzanso nawapeza ali m'tulo, pakuti maso ao analemeradi; ndipo sanadziwe chomyankha Iye.


Ndipo anawanenera fanizo lakuti ayenera iwo kupemphera nthawi zonse, osafooka mtima;


Za ichi ndinapemphera Ambuye katatu kuti chichoke kwa ine.


Ameneyo, m'masiku a thupi lake anapereka mapemphero ndi mapembedzero pamodzi ndi kulira kwakukulu ndi misozi kwa Iye amene anakhoza kumpulumutsa Iye muimfa, ndipo anamveka popeza anaopa Mulungu,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa