Marko 14:34 - Buku Lopatulika34 Ndipo ananena nao, Moyo wanga uli wa chisoni chambiri, kufikira imfa. Bakhalani pano, nimundikire. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 Ndipo ananena nao, Moyo wanga uli wa chisoni chambiri, kufikira imfa. Bakhalani pano, nimundikire. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Adaŵauza kuti, “Mumtima mwanga muli chisoni chachikulu chofa nacho. Inu khalani pompano, koma mukhale masotu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Iye anawawuza kuti, “Moyo wanga wagwidwa ndi chisoni chofa nacho. Khalani pano ndipo musagone.” Onani mutuwo |