Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 14:32 - Buku Lopatulika

32 Ndipo iwo anadza kumalo dzina lake Getsemani; ndipo ananena kwa ophunzira ake, Bakhalani pano, kufikira ndikapemphera.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

32 Ndipo iwo anadza kumalo dzina lake Getsemani; ndipo ananena kwa ophunzira ake, Bakhalani pano, kufikira ndikapemphera.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

32 Yesu adapita ndi ophunzira ake aja ku malo ena, otchedwa Getsemani. Tsono adauza ophunzirawo kuti, “Inu bakhalani pano, Ine ndikukapemphera.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

32 Ndipo anapita ku malo otchedwa Getsemani, ndipo Yesu anati kwa ophunzira ake, “Khalani pano pamene Ine ndi kupemphera.”

Onani mutuwo Koperani




Marko 14:32
10 Mawu Ofanana  

M'malo mwa chikondi changa andibwezera udani; koma ine, kupemphera ndiko.


Koma iye analimbitsa mau chilimbitsire, kuti, Ngakhale ndidzafa nanu, sindidzakana Inu. Ndipo onsewo anatero.


Ndipo ananena, Abba, Atate, zinthu zonse zitheka ndi Inu; mundichotsere chikho ichi; komatu si chimene ndifuna Ine, koma chimene mufuna Inu.


Ndipo anachokanso, napemphera, nanena mau omwewo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa