Marko 14:26 - Buku Lopatulika26 Ndipo ataimba nyimbo, anatuluka, namuka kuphiri la Azitona. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Ndipo ataimba nyimbo, anatuluka, namuka kuphiri la Azitona. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Tsono ataimba nyimbo yotamanda Mulungu, onse adatuluka nkumapita ku Phiri la Olivi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Atayimba nyimbo, anapita ku phiri la Olivi. Onani mutuwo |