Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 14:23 - Buku Lopatulika

23 Ndipo anatenga chikho, ndipo pamene adayamika, anapereka kwa iwo; ndipo iwo onse anamweramo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Ndipo anatenga chikho, ndipo pamene adayamika, anapereka kwa iwo; ndipo iwo onse anamweramo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Kenaka adatenga chikho, nathokoza Mulungu, nkuchipereka kwa ophunzirawo, naamwa onse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Kenaka anatenga chikho, nayamika nachipereka kwa iwo ndipo onse anamweramo.

Onani mutuwo Koperani




Marko 14:23
6 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene anatenga chikho, anayamika, napatsa iwo, nanena, Mumwere ichi inu nonse,


Ndipo pamene iwo analikudya, Iye anatenga mkate, ndipo pamene anadalitsa, ananyema, napereka kwa iwo, kuti, Tengani; thupi langa ndi ili.


Ndipo Iye anati kwa iwo, Ichi ndi mwazi wanga wa chipangano, wothiridwa chifukwa cha anthu ambiri.


Ndipo analandira chikho, ndipo pamene adayamika, anati, Landirani ichi, muchigawane mwa inu nokha;


Iye wakusamalira tsiku, alisamalira kwa Ambuye: ndipo iye wakudya, adya mwa Ambuye, pakuti ayamika Mulungu; ndipo iye wosadya, mwa Ambuye sakudya, nayamikanso Mulungu.


Chikho cha dalitso chimene tidalitsa, sichili chiyanjano cha mwazi wa Khristu kodi? Mkate umene tinyema suli chiyanjano cha thupi la Khristu kodi?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa