Marko 14:23 - Buku Lopatulika23 Ndipo anatenga chikho, ndipo pamene adayamika, anapereka kwa iwo; ndipo iwo onse anamweramo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Ndipo anatenga chikho, ndipo pamene adayamika, anapereka kwa iwo; ndipo iwo onse anamweramo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Kenaka adatenga chikho, nathokoza Mulungu, nkuchipereka kwa ophunzirawo, naamwa onse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Kenaka anatenga chikho, nayamika nachipereka kwa iwo ndipo onse anamweramo. Onani mutuwo |