Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 14:19 - Buku Lopatulika

19 Anayamba iwo kukhala ndi chisoni, ndi kunena naye mmodzimmodzi, kuti, Ndine kodi?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 Anayamba iwo kukhala ndi chisoni, ndi kunena naye mmodzimmodzi, kuti, Ndine kodi?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 Ophunzirawo adamva chisoni, nayamba mmodzimmodzi kumufunsa kuti, “Monga nkukhala ine?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 Iwo anamva chisoni, ndipo mmodzi ndi mmodzi anati kwa Iye, “Kodi ndine?”

Onani mutuwo Koperani




Marko 14:19
5 Mawu Ofanana  

Ndipo iwo anagwidwa ndi chisoni chachikulu, nayamba kunena kwa Iye mmodzimmodzi, Kodi ndine, Ambuye?


Ndipo pamene anaseama iwo kudya, Yesu anati, Ndithu ndinena ndi inu, Mmodzi wa inu adzandipereka Ine, ndiye wakudya ndi Ine pamodzi.


Ndipo anati kwa iwo, Mmodzi wa khumi ndi awiriwo, ndiye wakusunsa pamodzi ndi Ine m'mbale.


Ophunzira analikupenyana wina kwa mnzake, ndi kusinkhasinkha kuti ananena za yani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa