Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 13:37 - Buku Lopatulika

37 Ndipo chimene ndinena ndi inu ndinena kwa onse, Dikirani.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

37 Ndipo chimene ndinena ndi inu ndinena kwa onse, Dikirani.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

37 Zimene ndikunenazi, sindikuuza inu nokha ai, koma ndikuuza anthu onse kuti, ‘Khalani maso.’ ”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

37 Zimene ndikunena kwa inu, ndikunena kwa aliyense: ‘Khalani tcheru!’ ”

Onani mutuwo Koperani




Marko 13:37
5 Mawu Ofanana  

Chifukwa chake dikirani, pakuti simudziwa tsiku lake lakufika Ambuye wanu.


Yang'anirani, dikirani, pempherani: pakuti simudziwa nthawi yake.


Chifukwa chake dikirani; pakuti simudziwa inu nthawi yake yakubwera mwini nyumba, kapena madzulo, kapena pakati pausiku, kapena pakulira tambala, kapena mamawa;


Ndipo chitani ichi, podziwa inu nyengo, kuti tsopano ndiyo nthawi yabwino yakuuka kutulo; pakuti tsopano chipulumutso chathu chili pafupi koposa pamene tinayamba kukhulupirira.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa