Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 13:36 - Buku Lopatulika

36 kuti angabwere balamanthu nakakupezani muli m'tulo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

36 kuti angabwere balamanthu nakakupezani muli m'tulo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

36 Atha kudzabwera mwadzidzidzi, tsono asadzakupezeni muli m'tulo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

36 Ngati atabwera mwadzidzidzi, asadzakupezeni inu muli mtulo.

Onani mutuwo Koperani




Marko 13:36
14 Mawu Ofanana  

Usiku pamphasa panga ndinamfunafuna amene moyo wanga umkonda: Ndinamfunafuna, koma osampeza.


Ndinagona tulo, koma mtima wanga unali maso: Ndi mau a bwenzi langa mnyamatayo agogoda, nati, nditsegulire, mlongo wanga, wokondedwa wanga, nkhunda yanga, wangwiro wanga. Pakuti pamutu panga padzala mame, patsitsi panga pali madontho a usiku.


Alonda ake ali akhungu, iwo onse ali opanda nzeru; iwo onse ali agalu achete, osatha kuuwa; kungolota, kugona pansi, kukonda kugona tulo.


Ndipo pamene mkwati anachedwa, onsewo anaodzera, nagona tulo.


Ndipo anadza nawapeza iwo ali m'tulo, nanena ndi Petro, Simoni, ugona kodi? Unalibe mphamvu yakudikira ora limodzi kodi?


Ndipo anadzanso nawapeza ali m'tulo, pakuti maso ao analemeradi; ndipo sanadziwe chomyankha Iye.


Koma mudziyang'anire nokha, kuti kapena mitima yanu ingalemetsedwe ndi madyaidya ndi kuledzera, ndi zosamalira za moyo uno, ndi kuti tsiku ilo lingafikire inu modzidzimutsa ngati msampha;


Ndipo pamene ananyamuka pakupemphera anadza kwa ophunzira, nawapeza ali m'tulo ndi chisoni,


Mwa ichi anena, Khala maso wogona iwe, nuuke kwa akufa, ndipo Khristu adzawala pa iwe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa