Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 13:32 - Buku Lopatulika

32 Koma za tsiku ilo, kapena nthawi yake sadziwa munthu, angakhale angelo mu Mwamba, angakhale Mwana, koma Atate ndiye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

32 Koma za tsiku ilo, kapena nthawi yake sadziwa munthu, angakhale angelo m'Mwamba, angakhale Mwana, koma Atate ndiye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

32 “Koma za tsiku lake kapena nthaŵi yake, palibe amene amadziŵa. Angelo omwe akumwamba sadziŵa. Ngakhale Ineyo Mwanane sindidziŵa, amadziŵa ndi Atate okha basi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

32 “Palibe amene akudziwa za tsikulo kapena nthawi, ngakhale angelo akumwamba, kapena Mwana, koma Atate wokha.

Onani mutuwo Koperani




Marko 13:32
11 Mawu Ofanana  

Chifukwa chake dikirani, pakuti simudziwa tsiku lake, kapena nthawi yake.


Ndipo itapita nthawi yaikulu, anabwera mbuye wa akapolo awo, nawerengera nao pamodzi.


Koma pakati pa usiku panali kufuula, Onani, mkwati! Tulukani kukakomana naye.


Thambo ndi dziko lapansi zidzapita; koma mau anga sadzapita.


Koma anati kwa iwo, Sikuli kwa inu kudziwa nthawi kapena nyengo, zimene Atate anaziika mu ulamuliro wake wa Iye yekha.


Koma tsiku la Ambuye lidzadza ngati mbala; m'mene miyamba idzapita ndi chibumo chachikulu, ndi zam'mwamba zidzakanganuka ndi kutentha kwakukulu, ndipo dziko ndi ntchito zili momwemo zidzatenthedwa.


Chivumbulutso cha Yesu Khristu, chimene Mulungu anamvumbulutsira achionetsera akapolo ake, ndicho cha izi ziyenera kuchitika posachedwa: ndipo potuma mwa mngelo wake anazindikiritsa izi kwa kapolo wake Yohane;


Chifukwa chake kumbukira umo unalandira nunamvamo; nusunge nulape. Ukapanda kudikira tsono, ndidzafika ngati mbala, ndipo sudzazindikira nthawi yake ndidzadza pa iwe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa