Marko 13:31 - Buku Lopatulika31 Thambo ndi dziko lapansi zidzapita; koma mau anga sadzapita. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Thambo ndi dziko lapansi zidzapita; koma mau anga sadzapita. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Thambo ndi dziko lapansi zidzatha, koma mau anga sadzatha mphamvu konse.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Kumwamba ndi dziko lapansi zidzatha, koma mawu anga sadzatha.” Onani mutuwo |